Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Anthu onse adzadana nanu chifukwa cha dzina langa,+ koma amene adzapirire* mpaka mapeto ndi amene adzapulumuke.+

  • Afilipi 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndikuyesetsa kuti ndikwaniritse cholinga changa chokalandira mphoto.+ Mphoto imeneyi ndi kukakhala ndi moyo kumwamba+ ndipo Mulungu adzaipereka kwa anthu amene anawaitana kudzera mwa Khristu Yesu.

  • 2 Timoteyo 4:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndamenya nkhondo yabwino.+ Ndathamanga pa mpikisanowu mpaka pamapeto.+ Ndakhalabe ndi chikhulupiriro. 8 Panopa andisungira chisoti chachifumu cha olungama.+ Ambuye, woweruza wachilungamo,+ adzandipatsa mphotoyi pa tsikulo.+ Sikuti adzapatsa ine ndekha, koma adzapatsanso onse amene akhala akuyembekezera kuti iye adzaonekere.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena