-
2 Timoteyo 4:7, 8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndamenya nkhondo yabwino.+ Ndathamanga pa mpikisanowu mpaka pamapeto.+ Ndakhalabe ndi chikhulupiriro. 8 Panopa andisungira chisoti chachifumu cha olungama.+ Ambuye, woweruza wachilungamo,+ adzandipatsa mphotoyi pa tsikulo.+ Sikuti adzapatsa ine ndekha, koma adzapatsanso onse amene akhala akuyembekezera kuti iye adzaonekere.
-