Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Nanunso muzidziona ngati akufa pa nkhani ya uchimo, koma amoyo kwa Mulungu mwa Khristu Yesu.+

  • Akolose 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho chititsani ziwalo za thupi lanu+ padziko lapansi kukhala zakufa ku chiwerewere,* zinthu zodetsa, chilakolako chosalamulirika cha kugonana,+ kulakalaka zinthu zoipa komanso dyera limene ndi kulambira mafano.

  • 1 Yohane 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Aliyense amene ali wogwirizana ndi Yesu sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo.+ Amene ali ndi chizolowezi chochita tchimo ndiye kuti samukhulupirira* kapena kumudziwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena