Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chifukwa ndakupatsani chitsanzo kuti mmene ine ndachitira kwa inu, inunso muzichita chimodzimodzi.+

  • Aroma 16:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mundiperekere moni kwa Purisika ndi Akula,+ antchito anzanga potumikira Khristu Yesu. 4 Iwo anaika miyoyo yawo pachiswe chifukwa cha ine,+ ndipo si ine ndekha amene ndikuwayamikira, komanso mipingo yonse ya anthu a mitundu ina.

  • 1 Atesalonika 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho popeza timakukondani kwambiri,+ tinkafunitsitsa* kukuuzani uthenga wabwino wa Mulungu komanso kupereka miyoyo yathu yeniyeniyo+ kuti tikuthandizeni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena