Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 22:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Usatemberere* Mulungu+ kapena mtsogoleri* amene ali pakati pa anthu a mtundu wako.+

  • 2 Petulo 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 makamaka anthu amene amafunafuna anthu ena nʼcholinga choti awaipitse pogonana nawo+ ndiponso amene amanyoza olamulira.+

      Anthu amenewa saopa chilichonse komanso amamva zawo zokha. Iwo sachita mantha kulankhula zinthu zonyoza anthu amene Mulungu wawapatsa ulemerero.

  • 3 Yohane 9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mpingo wanu ndinaulembera kalata, koma Diotirefe amene amakonda kukhala woyamba pakati panu,+ salemekeza chilichonse chimene tanena.+ 10 Nʼchifukwa chake ndikadzabwera, ndidzaulula zimene akuchita pofalitsa mabodza onena za ife.+ Ndipo chifukwa chosakhutira ndi zimenezi, amakana kulandira abale+ mwaulemu. Komanso anthu amene amafuna kuwalandira, amayesa kuwatsekereza ndiponso kuwachotsa mumpingo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena