Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Zabwino zimene munthu wolungama ankachita zikakumbukiridwa* amadalitsidwa,+

      Koma dzina la anthu oipa lidzawola.+

  • Aheberi 10:26, 27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ngati tikuchita machimo mwadala pambuyo podziwa choonadi molondola,+ palibenso nsembe ina imene ingaperekedwe chifukwa cha machimo athuwo.+ 27 Koma pali chiyembekezo china choopsa cha chiweruzo, ndiponso mkwiyo woyaka moto umene udzawononge otsutsawo.+

  • Chivumbulutso 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Amene ali ndi makutu amve+ zimene mzimu ukunena ku mipingo kuti: Amene wapambana pankhondo+ sadzakhudzidwa ndi imfa yachiwiri.’+

  • Chivumbulutso 20:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Wosangalala komanso woyera ndi aliyense amene akuuka nawo pa kuuka koyamba.+ Imfa yachiwiri+ ilibe ulamuliro pa amenewa.+ Koma adzakhala ansembe+ a Mulungu ndi a Khristu, ndipo adzalamulira monga mafumu limodzi ndi Khristu zaka 1,000.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena