Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g95 12/8 tsamba 32
  • Zisonyezero za Voliyumu 76 ya Galamukani!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Voliyumu 76 ya Galamukani!
  • Galamukani!—1995
  • Timitu
  • ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI
  • CHIPEMBEDZO
  • CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA
  • LINGALIRO LA BAIBULO
  • MAIKO NDI ANTHU
  • MAUNANSI A ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • SAYANSI
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZINYAMA NDI ZOMERA
  • ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE
  • ZOSIYANASIYANA
Galamukani!—1995
g95 12/8 tsamba 32

Zisonyezero za Voliyumu 76 ya Galamukani!

ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI

Kuba—Kulekeranji?, 7/8

Kukhala Bwenzi la Mulungu, 8/8, 12/8

Kukonza Moyo, 1/8

Kuloŵa Msanga mu Ukwati, 5/8

Kupeza Zovala Zoyenera, 2/8

Kutaya Mimba Ndiko Yankho?, 3/8

Kuvutitsidwa ndi Amuna Kapena Akazi, 9/8

Makolo Ochita Molakwa, 6/8

Nchifukwa Ninji Aliyense Akuloŵa mu Ukwati?, 11/8

Ndiphunzire Kudzitetezera?, 10/8

Umathanyula, 2/8, 3/8, 4/8

CHIPEMBEDZO

Bungwe la World Council of Churches, 4/8

Chimene Matchalitchi Anakhalira Chete, 9/8

Kodi Adzalalikira Khomo ndi Khomo?, 3/8

Kodi Siali a Dziko Lapansi?, 1/8

Kufunafuna Waluso Wamkulu Koposa, 11/8

Mabishopu a Italy Akuda Nkhaŵa, 3/8

Krisimasi—Chiyambi Chake, 12/8

Mapeto a Dziko, 7/8

Tchalitchi cha Katolika mu Afirika, 1/8

CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA

Chipululutso cha Zachuma, 5/8

Kuloŵa m’Ngongole Kumathandiza?, 6/8

LINGALIRO LA BAIBULO

Chifuno cha Moyo, 5/8

Chigololo—Kukhululukira Kapena Kusakhululukira?, 8/8

Kodi Mpikisano m’Maseŵero Ngwoipa?, 12/8

Kodi Zimene Mumakhulupirira Zili Nkanthu?, 7/8

Kukhululukira ndi Kuiŵala—Kodi Nkotheka Motani?, 6/8

Mbali Yanu m’Mapemphero Anu, 9/8

Miyezo ya Mulungu ndi Yosafikirika?, 10/8

Mulungu Amakondwa Kutiona Tikuvutika?, 3/8

Ndani Amapita Kumwamba?, 1/8

Umbeta, 2/8

MAIKO NDI ANTHU

Kuchokera ku Mabotolo Kukhala Mkanda (Nigeria), 11/8

Kumene Ziombankhanga Zimaulukira Kukadya Nsomba (Alaska), 12/8

Sukulu ya mu Afirika, 10/8

Tanthauzo la Nyawu (Afirika), 8/8

MAUNANSI A ANTHU

Ana Osoŵa, 2/8

Kodi Mumaŵerengera Agogo?, 7/8

Mabanja a Kholo Limodzi, 10/8

MBONI ZA YEHOVA

Chimene Analankhulira Mopanda Mantha, 9/8

Chipolopolo Chinasintha Moyo Wanga (G. Williams), 11/8

Kumene Ndalama Zimakhala m’Mitengo, 7/8

Kupanga Ophunzira Enieni Lerolino, 1/8

Kusamalira Ovutika ndi Tsoka la ku Rwanda, 1/8

Lingaliro Langa la Ntchito ya Madokotala Lasintha, 2/8

Liwu Lomvekapo Lokha Kuli Chete?, 9/8

Mabuku Ayamikiridwa m’Maiko Amene Anali Soviet Union, 6/8

Ulendo Wobwereza ku Russia, 3/8

Zaka Zoposa 40 Pansi pa Chiletso cha Komyunizimu (J. Hálová), 5/8

SAYANSI

Iceman, 5/8

Miyala Imene Imauluka, 12/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Chakudya Chanu Chilidi Chomanga Thupi?, 3/8

Fungo Loipa la m’Kamwa, 7/8

Khungu la mu Mtsinje, 10/8

Kudwala kwa Mkazi Ali Pafupi Kusamba, 8/8

Kumene AIDS Uli Mliri Waukulu, 8/8

Kupsa ndi Ntchito, 1/8

Kusiyana m’Zathanzi kwa Padziko Lonse, 4/8

Miyoyo Mamiliyoni Ambiri Ikuthera mu Utsi (Kusuta), 6/8

Nchifukwa Ninji Moyo Uli Waufupi Motere?, 11/8

Nthenda za m’Chakudya, 12/8

Nyengo Yoleka Kusamba, 3/8

Pamene Sikudzakhalanso Matenda, 4/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Chipembere, 8/8

Chiswe—Bwenzi Kapena Mdani?, 6/8

“Mtengo wa Moyo” Wodabwitsa wa Afirika (Mulambe), 4/8

Ng’ona, 4/8

Njati ya m’Madzi—Yokhulupirika ndi Yothandiza, 8/8

Nyalugwe, 4/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Ana Osoŵa, 2/8

Chakudya Chokwanira kwa Onse! 11/8

Juga—Kumwerekera Komakula, 10/8

Kodi Ano Ndiwo Masiku Otsiriza?, 5/8

Kodi Maiko Olemera Adzadyerera Osauka Nthaŵi Zonse?, 12/8

Kodi Munthu Adzakhoza Kulimbana ndi Masoka?, 8/8

Kusiyana m’Zathanzi kwa Padziko Lonse, 4/8

Kuvumbula Zoipa za Nazi?, 9/8

Maiko Osauka Akhala Kotayira Zinyalala, 12/8

Maunyolo ndi Misozi ya Ukapolo, 6/8

1945-1995, 9/8

ZOSIYANASIYANA

Kunyong’onyeka, 2/8

Kuzengereza—Mbala ya Nthaŵi, 4/8

Njira ya Mwana Yoyendera, 12/8

Mpunga—Wophika Kapena Wosaphika?, 2/8

[Bokosi patsamba 32]

Ngati mungafune chidziŵitso chowonjezereka kapena phunziro la Baibulo la panyumba laulere, chonde lemberani Watch Tower kapena kukeyala yoyenera pandandanda ya patsamba 5.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena