Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • go tsamba 1-2
  • Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa
  • Boma Lathu la Dziko Likudza’lo—Ufumu wa Mulungu
Boma Lathu la Dziko Likudza’lo—Ufumu wa Mulungu
go tsamba 1-2

Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa

Boma Lathu la Dziko Likudza’lo—Ufumu wa Mulungu

Kuyang’ana Patsogola’pa M’Kuunika Kowala kwa Maulosi a Baibulo Amene Atsala Pang’ono Kukwaniritsidwa mu Mpangidwe wa Ulamuliro Umodzi Umene Udzakwaniritsa Zosowa ndi Zokhumba Zathu Zonse

“Mulungu ndiye Mfumu ya dziko lonse lapansi; yimbirani ndi chilangizo. Mulungu ndiye Mfumu ya amitundu: Mulungu akhala pa mpando wachifumu wake woyera.”—Salmo 47:7, 8.

LOPEREKEDWA kwa Mulungu amene nthawi yake yachimwemwe yafika yakuti alowetse m’malo mwa ulamuliro waumunthu wosakaza’wo ndi wa iye mwini wokhala ndi boma lolungama limene anthu opsyinjika a mafuko onse aliyembekezera kwa nthawi yaitali.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena