Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • tp tsamba 1-2
  • Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa
  • Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
tp tsamba 1-2

Mutu wa Buku Lino/​Tsamba la Ofalitsa

Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?

Anthu kulikonse amafuna mtendere weniweni ndi chisungiko. Amalakalaka kupeza mpumulo ku mavuto ambiri amene amawasautsa. Kodi pali chothetsera mavutowa chosatha? Bukhu iri lafalitsidwa ndi chitsimikizo chakuti chiripo, ndi kuti mwamsanga mtendere weniweni ndi chisungiko zidzakhala zenizeni pa dziko lonse lapansi. Chiri chikhumbo chathu chowona mtima kuti mwa kuliwerenga mudzapeza chiyembekezo cholimba ndi chitsimikiziritso chosangalatsa mtima chonena za chimene chiri m’tsogolo kaamba ka onse amene amakonda chilungamo.

—Afalitsi

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena