Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • cf tsamba 1
  • ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
  • ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
cf tsamba 1
Buku lakuti ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga.’

‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’

Kodi nthawi zina mumaona kuti simukudziwa zoyenera kuchita ndipo mukufunika munthu woti akuthandizeni? Aliyense akufunika kutsogoleredwa ndi Yesu Khristu chifukwa ndi Mtsogoleri amene Mulungu anatipatsa. Yesu anati: “Ine ndine m’busa wabwino, nkhosa zanga ndimazidziwa ndipo nazonso zimandidziwa.” (Yohane 10:14) Kodi M’busa Wabwino ameneyu mumamudziwadi? Kodi mumadziwa makhalidwe ake, uthenga wake, ntchito imene ankagwira mwakhama ndiponso chikondi chake? Bukuli likuthandizani kuti mumudziwe bwino kwambiri Yesu ndiponso kuti muzimutsatira mosamala kwambiri.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena