Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w96 3/15 tsamba 32
  • Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya
  • Nsanja ya Olonda—1996
Nsanja ya Olonda—1996
w96 3/15 tsamba 32

Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya

“Mphatso iliyonse yabwino, ndi chininkho chilichonse changwiro” zimachokera kwa Mulungu, Atate wathu wakumwamba. (Yakobo 1:17) Mphatso yoposa zonse imene Mulungu wapereka kwa anthu ochimwa ndiyo makonzedwe a chipulumutso chawo mwa Mwana wake wobadwa yekha, Yesu Kristu. Imfa ya Yesu monga Momboli wathu imatheketsa moyo wosatha padziko lapansi la paradaiso. Pa Luka 22:19, timalamulidwa kukumbukira imfa yake.

Mboni za Yehova zikukupemphani ndi mtima wonse kuti mukakhale nazo pamodzi posunga lamulo la Yesulo. Chochitika chapachaka chimenechi chidzachitidwa dzuŵa litaloŵa padeti logwirizana ndi Nisani 14 pa kalenda ya mwezi ya Baibulo, pamene padzakhala pa Lachiŵiri, April 2, 1996. Sungani deti limeneli kuti musadzaiŵale. Mboni za Yehova zakwanuko zingakuuzeni za malo enieni ndi nthaŵi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena