Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w01 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2001

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2001
  • Nsanja ya Olonda—2001
  • Timitu
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBIRI YA MOYO WANGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—2001
w01 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2001

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

Buku Lokhala ndi Mabuku Onse a M’Baibulo, 5/1

Cyril ndi Methodius​—Otembenuza, 3/1

Kuyamikira Baibulo la New World Translation, 11/15

Kumvetsa Baibulo, 7/1

Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa, 2/15

N’kuphunziriranji Baibulo, 7/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Kodi akristu oona ayenera kuchiona motani chizoloŵezi chofala chopatsana ulere mapulogalamu ogulitsa a pakompyuta? 2/15

Kodi Danieli anali kuti pamene Ahebri atatu aja anawayesa kuti alambire fano lagolide? (Da 3), 8/1

Kodi kudzoza “Malo Opatulikitsa” kunachitika liti? (Da 9:24), 5/15

Kodi kulambira Yehova “mumzimu” kumatanthauzanji? (Yoh 4:24), 9/15

Kodi njoka ija m’munda wa Edene inalankhula motani? 11/15

Kodi Tiyenera Kupempherera Munthu Wochotsedwa? (Yer 7:16),12/1

Kodi Yehova anapangana naye pangano Abrahamu ali ku Uri kapena ku Harana? 11/1

Kodi Yobu anavutika kwa nthaŵi yaitali motani? 8/15

Kulowa mpumulo wa Yehova (Aheb. 4:9-11), 10/1

“Kupembedza mafano kosaloleka,” (1Pe 4:3), 7/15

Mitengo yonyamulira likasa la chipangano (1Maf.8:8), 10/15

“Miyamba” (2Pe 3:13) ndi “kumwamba” (Chiv. 21:1), 6/15

Mkazi wachikristu ndi zochitika za maholide, 12/15

N’chifukwa chiyani kuli kofunika kwa Akristu kuulula machimo awo kwa akulu mu mpingo? 6/1

Zinthu zonse zinalengedwa “kwa” Yesu motani? (Akol 1:16), 9/1

MBIRI YA MOYO WANGA

Anapirira ‘Kufikira Chimaliziro’ (L. Swingle), 7/1

Kuchirikizidwa ndi Yehova (F. Lee), 3/1

Kukatumikira Kulikonse Kumene Ndinkafunika (J. Berry), 2/1

Kutsatabe Njira ya Yehova (L. Valentino), 5/1

Kutumikira ndi Moyo Wonse Mosasamala Kanthu za Mayesero (R. Lozano), 1/1

Kuunika Kwauzimu Kukuwala ku Middle East (N. Salem), 9/1

Kuvomera Yehova Akamatipempha (M. Zanardi), 12/1

Moyo Waulemerero Potumikira Yehova (R. Kurzen), 11/1

Ndimayamikira Chifukwa Chokumbukira Zinthu Zamtengo Wapatali! (D. Caine), 8/1

Tinamuyesa Yehova (P. Scribner), 7/1

Tinkachitira Zinthu Limodzi (M. Barry), 4/1

Wosangalala ndi Wothokoza Ngakhale pa Vuto Losautsa Mtima (N. Porter), 6/1

“Yehova Wandichitira Zabwino Zambiri!”(K. Klein), 5/1

Zochitika Zosayembekezeka (E. & H. Beveridge), 10/1

MBONI ZA YEHOVA

Analandira Satifiketi Chifukwa cha Kuchita Bwino (Congo [Kinshasa]), 8/15

Anapambana Chizunzo cha Nazi, 3/15

Apambana Mlandu M’khoti Lapamwamba la Federal Constitution (Germany), 8/15

Dokotala wa Maso Afesa Mbewu (Ukraine, Israel), 2/1

France, 8/15, 9/1

Kale Tinali Mimbulu​—Tsopano Ndife Nkhosa! 9/1

Kenya, 2/15

Kodi Ntchito Iyi Ingakhale Yabwino Kwambiri kwa Inu? (Utumiki wa pa Beteli), 3/15

Kumaliza Maphunziro a Gilead, 6/15, 12/15

Kusamalirana Muubale Wapadziko Lonse (Othawa Nkhondo), 4/15

Kuthandiza Achinyamata, 7/15

Madzi Opatsa Moyo ku Andes, 10/15

Misonkhano ya Chigawo ya “Akuchita Mawu a Mulungu,” 1/15

Misonkhano ya Chigawo ya “Aphunzitsi a Mawu a Mulungu,” 2/15

Misonkhano Yaikulu Ndi Umboni Wosangalatsa wa Ubale Wathu, 9/15

Mmene Bungwe Lolamulira Limasiyanirana ndi Bungwe Lalamulo, 1/15

Msonkhano Wapachaka wa 2000, 1/15

“Ntchito Yaukatswiri” (Seŵero la Pakanema), 1/15

Sitinali Tokha Pamene Chikhulupiriro Chathu Chinali Kuyesedwa (Magazi), 4/15

‘Thokozani Mboni za Yehova Chifukwa cha Ufulu Wachipembedzo,’ 5/15

“Tidzaonana mu Ufumu wa Mulungu” (F. Drozg), 11/15

Timachita Zonse Zomwe Tingathe! (Amishonale), 10/15

“Tsiku Lokambirana za Zipembedzo” (Sukulu za ku Poland), 11/1

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Anthu Sakumvetsetsani? 4/1

Chikhulupiriro Chenicheni, 10/1

Gonjetsani Zinthu Zokulepheretsani Kupita Patsogolo, 8/1

Kodi Mulidi Ololera? 7/15

‘Kugwiritsa Ntchito Nthaŵi Moyenera,’ 5/1

Kukayika, 7/1

Kukulitsa Khalidwe Labwino, 1/15

Kulapa, 6/1

Kumvera​—Phunziro Lofunika Paubwana, 4/1

Kupeŵa Matenda a Mtima Wauzimu, 12/1

Kupitirizabe Polefulidwa! 2/1

Kusankha Mwanzeru, 9/1

Kuthandiza Akazi Amasiye, 5/1

Kwaniritsani Zomwe Ana Anu Amafunikira! 12/15

Limbikitsani Chikhulupiriro mwa Yehova, 6/1

‘Madalitso Ali pa Wolungama,’ 7/15

“Madalitso a Yehova Alemeretsa,” 11/1

“Motero Thamangani,” 1/1

Mumatani Pakachitika Chinyengo, 11/15

Mungachite Moyenera Ngakhale Sanakulereni Bwino, 4/15

‘Ndi Nzeru Masiku Athu Adzachuluka’ (Miy. 9), 5/15

Samalirani Ana ndi Akazi Amasiye, 6/15

Tetezani Chikumbumtima, 11/1

Udani​—Woyenera ndi Wosayenera, 2/15

‘Wodala Munthu Wopeza Nzeru’’ (Miy. 8), 3/15

Yendani ‘M’njira Yoongoka’ (miy. 10), 9/15

Zomwe Munazoloŵera Kuchita, 8/1

Zoyenera Kuchita Ngati Mukuvutika Maganizo, 4/15

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

Abrahamu Anali Chitsanzo cha Chikhulupiriro, 8/15

Anthu Obwezeretsedwa a Yehova Akum’tamanda Padziko Lonse Lapansi, 2/15

Chikristu Choona Chikupambana! 4/1

Chipulumutso Kwa Osankha Kuunika, 3/1

Chisangalalo Kwa Oyenda M’kuunika, 3/1

‘Funafunani Mtendere ndi Kuulondola,’ 9/1

Funafunani Yehova Lisanadze Tsiku La Mkwiyo Wake, 2/15

Ganizirani Ntchito Zodabwitsa za Mulungu, 4/15

Khalanibe Osasunthika Ngati Oona Wosaonekayo! 6/15

Khalani Ndi Chikhulupiriro Monga cha Abrahamu! 8/15

Khalani ndi Mtima woopa Yehova, 12/1

Khalani ndi Mtima Wovomerezeka kwa Yehova, 10/15

Kodi Chikondi Chanu N’chosefukira Motani? 1/1

Kodi Madalitso A Yehova Adzakupezani? 9/15

Kodi Mtendere wa Kristu Ungachite Motani Ufumu M’mitima Yathu? 9/1

Kodi Mukuchita Mogwirizana Ndi Kudzipatulira Kwanu? 2/1

Kodi Mutha “Kusiyanitsa Chabwino ndi Choipa”? 8/1

Kodi Mwana “Wosakaza” Mungamuthandize Bwanji? 10/1

Kodi Mwapanga Choonadi Kukhala Chanuchanu? 2/1

Kondwerani ndi Mulungu Wachimwemwe, 5/1

Kondwerani Nthaŵi Zonse Potumikira Yehova, 5/1

Kondwerani Pakuti Mwadziŵa Yehova, 7/1

Kugonjetsa Kufooka Kwaumunthu, 3/15

Kulani M’chikondi, 1/1

Kumanga Banja Lolimba Mwauzimu, 5/15

Kupita Patsogolo Kukagonjetsa Komaliza! 6/1

Limbikirani Ntchito Yotuta! 7/15

Madalitso A Yehova Amatilemeretsa, 9/15

Malangizo a Mulungu Othandiza Posankha Wokwatirana Naye, 5/15

Mankhwala Omwe Angathandize Kuthetsa Nkhaŵa, 12/15

‘Mawu a Yehova Anapitirizabe Kukula,’ 4/1

Musakhale Akumva Oiŵala, 6/15

Musasiye Kuchita Zabwino, 8/15

Ndani Adzatisiyanitsa ndi Chikondi cha Mulungu? 10/15

“Ngati Mulungu Ali ndi Ife, Adzatikaniza Ndani?” 6/1

Onetsani Kuti Mukupita Patsogolo, 8/1

Opani Yehova ndi Kusunga Malamulo Ake, 12/1

Oyang’anira ndi Atumiki Otumikira Amaikidwa Mwateokalase, 1/15

Pezani Chimwemwe mwa Kukhala Wopatsa! 7/1

“Phunzirani kwa Ine,” 12/15

Samalirani Mzimu ndi Kukhala ndi Moyo! 3/15

Sangalalani Ndi Ntchito Yotuta! 7/15

Tamandani Yehova Chifukwa cha Ntchito Zake Zazikulu! 5/15

Taonani Wochita Zinthu Zodabwitsa! 4/15

Tchinjirizani Mtima Wanu, 10/15

Tsanzirani Yehova Pophunzitsa Ana Anu, 10/1

Tsiku la Yehova Lopereka Chiŵeruzo Layandikira! 2/15

‘Valani Kuleza Mtima,’ 11/1

Yehova Amatidziŵitsa Kuŵerenga Masiku Athu, 11/15

Yehova Ndi Mulungu Woleza Mtima, 11/1

Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu, 11/15

Yenderani Limodzi ndi Gulu la Yehova, 1/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Ahasimoni, 6/15

Asikuti, 11/15

Chikhulupiriro cha Nowa Chimatsutsa Dziko Lapansi, 11/15

Chimwemwe, 3/1

Chitetezo M’dziko Loopsali, 2/1

Chokhalitsa Kuposa Golide, 8/1

Enoke Anayenda ndi Mulungu, 9/15

“Khalidwe Lobisika Lowononga Thanzi” (Zolaula za pa Intaneti), 4/15

Kodi Abambo a Tchalitchi Anachirikiza Choonadi cha Baibulo? 4/15

Kodi Chilipo Chimene Chingagwirizanitse Anthu? 9/15

Kodi Chofunika Kwambiri N’chiyani? 9/15

Kodi Mungakhulupirire Miyezo ya Ndani? 6/1

Kodi Mungapange Dziko Lapansi Kukhala Malo Abwinopo? 10/15

Kodi Munthu Akamwalira Amakhala ndi Moyo Kwinakwake? 7/15

Kukhulupirira Mizimu, 5/1

Kuona Ndalama M’njira Yoyenera, 6/15

Kuvutika, 5/15

Lamulo la Chikhalidwe Likugwirabe Ntchito, 12/1

Mabala a Nkhondo, 1/1

‘Mankhwala Opaka M’maso Mwanu!’ 12/15

Maziko a Zimene Mumakhulupirira, 8/1

Mdyerekezi, 9/1

Mitengo Imene Imakhalitsa, 7/1

“Mitsempha Yako Idzalandirapo Moyo,” 2/1

‘M’kuunika Kwanu Tidzaona Kuunika,’ 12/1

Mmene Mungapambanire Paunyamata Wanu, 8/15

Mutha Kukhala ndi Chikhulupiriro Chenicheni, 10/1

Mzimu Wosafa? 7/15

“Ndikachita Apilo kwa Kaisara!”

Opaleshoni Yopanda Magazi, 3/1

Origen​—Kodi Chiphunzitso Chake Chinakhudza Tchalitchi Motani? 7/15

Paradaiso Wauzimu, 3/1

Paulo Alinganiza Zopereka Zothandizira Oyera Mtima Pa Mavuto, 3/15

‘Taonani Khamu Lalikulu!’ 5/15

Uthenga Wabwino wa Ufumu, 4/1

Yamikirani Ndipo Sangalalani, 9/1

Zinthu Zowononga Mitengo, 11/1

Zomwe Tingaphunzire ku Mtengo wa Kanjedza, 10/1

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

2/1, 4/1, 5/1, 6/1, 8/1, 10/1, 12/1

YEHOVA

Limbikitsani Chikhulupiriro mwa Yehova, 6/1

“Madalitso a Yehova Alemeretsa,” 11/1

YESU KRISTU

Kodi Yesu Amapulumutsa Motani? 11/15

Kuuka, 3/15

Yesu Weniweni, 12/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena