Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2008
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2008
w08 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2008

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:

April 21-27, 2008

Khalani Ololera Koma Mosapitirira Malire

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 8, 177

April 28, 2008–May 4, 2008

Sangalalani mu Ukwati Wanu

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 117, 89

May 5-11, 2008

Yehova Amamva Kulira Kwathu Ndipo Amatithandiza

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 58, 135

May 12-18, 2008

“Kodi Wanzeru ndi Womvetsa Zinthu Ndani Pakati pa Inu?”

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 106, 51

May 19-25, 2008

Kodi Mumaona Anthu Mmene Yehova Amawaonera?

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 127, 213

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Mosiyana ndi zimene anthu ambiri amaganiza, pali zifukwa zabwino zimene Akhristu afunikira kukhala ololera. Kodi zifukwazo ndi zotani? Ndipo kodi muyenera kuchita chiyani kuti mukhale ololera muukwati wanu?

Nkhani Zophunzira 3 MASAMBA 12-16

N’chifukwa chiyani tili ndi chikhulupiriro chakuti Yehova amamva kulira kwathu ndipo amatithandiza? Nkhani imeneyi ikuyankha funsoli ndipo ikusonyeza mmene tingapezere mphamvu kuti tipirire mayesero.

Nkhani Zophunzira 4, 5 MASAMBA 21-29

Nkhani ziwirizi zitithandiza kuti tiziona anthu moyenera ndi kupewa chizolowezi chimene ambiri ali nacho chokonda kuweruza anzawo. Ndipo tiona kusiyana pakati pa munthu wanzeru ndi wopanda nzeru.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Kufalitsa Uthenga Wabwino M’mapiri a Andes

TSAMBA 16

Pangano Lofunika Kwambiri

TSAMBA 19

Mawu a Yehova Ndi Amoyo​—Mfundo Zazikulu za M’buku la Luka

TSAMBA 30

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena