Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2008
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2008
w08 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2008

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:

August 4-10, 2008

Zinthu Zimene Tiyenera Kuthawa

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 139, 146

August 11-17, 2008

Makhalidwe Amene Tiyenera Kutsatira

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 42, 54

August 18-24, 2008

Gonjerani Ulamuliro wa Yehova

TSAMBA 18

NYIMBO ZOIMBA: 47, 2

August 25-31, 2008

Musasiye ‘Chikondi Chimene Munali Nacho Poyamba’

TSAMBA 22

NYIMBO ZOIMBA: 201, 132

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 7-15

Timakhulupirira kuti Mulungu amatikonda. Umboni wa zimenezi ndi wakuti iye watiuza zinthu zinayi zimene Akhristufe tiyenera kuzithawa. Kodi zinthu zimenezi ndi ziti, ndipo tingazithawe bwanji? Komanso, Baibulo limatchula zinthu 7 zimene tiyenera kuzitsatira. Kodi zinthu zimenezi ndi ziti, ndipo tingazitsatire bwanji?

Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 18-22

Mzimu wofuna kudziimira pawekha ndi wofala m’dzikoli. Ndiyeno, kodi tingatani kuti tizilemekeza ulamuliro, makamaka wa Yehova? Nkhani imeneyi itithandiza kudziwa mmene tingachitire zimenezi, komanso mmene tingapewere mzimu wofuna kudziimira pawekha umene Satana amalimbikitsa.

Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 22-26

Nkhani yophunzira imeneyi itithandiza kuganizira zimene zinatichititsa kuyamba choonadi ndiponso kukonda Yehova. Ikupereka malangizo a zimene munthu angachite kuti ayambe kukondanso Yehova ndi choonadi, ngati chikondicho chakhala chikuzirala.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Tingakhale Amphamvu Ngakhale Tili ndi Zofooka

TSAMBA 3

Kodi Ndinu Wokonzeka Kufotokoza za Chikhulupiriro Chanu?

TSAMBA 16

Kodi Yesu Anali Kunena za Moto wa Helo?

TSAMBA 27

Mafunso Ochokera kwa Owerenga

TSAMBA 28

Mawu a Yehova Ndi Amoyo Mfundo Zazikulu za M’kalata ya Aroma

TSAMBA 29

Inali Nzeru Yothandiza

TSAMBA 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena