Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w09 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2009
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2009
w09 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

August 3-9, 2009

Khalani Achangu pa Nyumba ya Yehova

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 31, 118

August 10-16, 2009

Khalani “Achangu pa Ntchito Zabwino”

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 30, 181

August 17-23, 2009

Lankhulani Zoona kwa Mnansi Wanu

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 192, 170

August 24-30, 2009

Mdindo Wokhulupirika ndi Bungwe Lake Lolamulira

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 51, 114

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 7-15

Mafumu anayi a Yuda anachita zazikulu kwambiri pochirikiza kulambira koona. Kodi chitsanzo chawo chingatiphunzitse chiyani pa nkhani ya changu chathu potumikira Yehova? Nkhani ziwirizi n’zosangalatsa ndiponso zili ndi malangizo abwino zedi.

Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 16-20

Tsiku ndi tsiku pamachitika zinthu zomwe zingatichititse kuganiza kuti chidule n’kungonama basi. Apo ayi tingaone kuti tikanena zoona ndiye kuti sitinam’ganizire winawake, kapenanso tinganene dala zinthu zoti wina asazimvetse. N’chifukwa chiyani Akhristu oona ayenera kuyesetsa kuti asamachite zimenezi? Kodi n’chiyani chingakuthandizeni pa nkhani imeneyi?

Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 20-24

Anthu a Mulungu amalemekeza kwambiri gulu la kapolo wokhulupirika ndi wanzeru. Koma kodi pali mgwirizano wotani pakati pa gulu limeneli ndi Bungwe Lolamulira? Ndipo kodi Malemba amati Yehova amatipatsa bwanji chakudya chauzimu masiku ano? Komanso kodi tiyenera kuwaona motani anthu amene amadya zizindikiro za pa Chikumbutso? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa mwatsatanetsatane.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Kodi Ndingam’bwezere Chiyani Yehova?

TSAMBA 3

Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala ndi Umbeta

TSAMBA 25

Muzipatsa Ena Ntchito Zina

TSAMBA 28

Mafunso Ochokera kwa Owerenga

TSAMBA 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena