Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w09 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2009
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2009
w09 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

October 26, 2009–November 1, 2009

Khalani ndi Maganizo a Khristu

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 62, 66

November 2-8, 2009

Khalani Omvera Ndiponso Olimba Mtima Ngati Khristu

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 8, 107

November 9-15, 2009

Chikondi cha Khristu Chimatilimbikitsa Kukonda Ena

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 89, 35

November 16-22, 2009

Maphunziro Ochokera kwa Mulungu Ndi Opambanadi

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 91, 59

November 23-29, 2009

Kodi Mumayamikira Zimene Yehova Wachita Kuti Akupulumutseni?

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 55, 153

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1-3 TSAMBA 7-20

Tikudziwa kuti Yesu anapereka chitsanzo kwa Akhristu m’njira zambiri. Nkhani izi zikufotokoza bwino maganizo a Yesu ndiponso zochita zake. Muona mmene chitsanzo chake chingakuthandizireni m’banja mwanu, mumpingo ndiponso polimbana ndi mavuto.

Nkhani Yophunzira 4 TSAMBA 21-25

Kodi mumayamikira kwambiri choonadi chimene mwaphunzira m’Mawu a Mulungu? Nkhani imeneyi itithandiza kuganizira madalitso amene tapeza chifukwa cha maphunziro ochokera kwa Mulungu. Ikufotokozanso madalitso amene timapeza tikadzimana zinthu zina chifukwa cha uthenga wabwino.

Nkhani Yophunzira 5 TSAMBA 25-29

Kodi Yehova wachita chiyani kuti atipulumutse ku uchimo ndi imfa? Kodi anadzimana chiyani kuti zimenezi zitheke? Kudziwa mayankho a mafunso amenewa, kungatithandize kukhala ndi mtima woyamikira ndiponso kungatilimbikitse kuti timusonyeze Yehova kuti timayamikira kwambiri chiyembekezo cha chipulumutso chimene Iye ndi Mwana wake atipatsa.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Kodi Chipembedzochi Ndi Changa Kapena cha Makolo Anga?

TSAMBA 3

Ndinapeza Cholinga cha Moyo

TSAMBA 30

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena