Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

June 28, 2010–July 4, 2010

Amuna, Kodi Mumagonjera Khristu Monga Mutu Wanu?

TSAMBA 8

NYIMBO ZOIMBA: 5, 42

July 5-11, 2010

Akazi, N’chifukwa Chiyani Muyenera Kugonjera Amuna Monga Mutu?

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 3, 6

July 12-18, 2010

Abale, Feserani Mzimu Ndipo Yesetsani Kuti Muyenerere Udindo

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 45, 11

July 19-25, 2010

Musamvetse Chisoni Mzimu Woyera wa Yehova

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 38, 26

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 8-17

Nkhani yophunzira yoyamba ikufotokoza chifukwa chake amuna afunika kugonjera Mutu wawo, yemwe ndi Khristu ndiponso kumutsanzira pochita zinthu ndi ena. Nkhani yachiwiri ikufotokoza mmene akazi achikhristu ayenera kuonera mawu akuti: “Mutu wa mkazi ndi mwamuna.”

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 MASAMBA 24-32

Masiku ano, anthu ambiri safuna kuchita zinthu modzimana pofuna kuthandiza ena. Nkhani yoyamba yakonzedwa n’cholinga chothandiza makamaka amuna obatizidwa kuti aone mmene akuchitira pa nkhani yodzimana ndiponso ngati ali ndi mtima wofuna kukhala atumiki othandiza kapena akulu. Nkhani yachiwiri ikufotokoza mmene tingapewere kumvetsa chisoni mzimu woyera wa Mulungu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Akhristu Oyambirira Ndiponso Milungu ya Aroma 3

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kulemekeza Okalamba? 6

Khalanibe Olimba Mwauzimu Mukamasamalira Wachibale Amene Akudwala 17

Mumzinda wa Harana Munkachitika Zinthu Zambiri 20

Mafunso Ochokera kwa Owerenga 21

Pitirizani Kuphunzitsa Luntha Lanu la Kuzindikira 22

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena