Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

October 25-31, 2010

Muzifunafuna Madalitso a Yehova ndi Mtima Wonse

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 1, 38

November 1-7, 2010

Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Kugwirizana

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 20, 53

November 8-14, 2010

Mgwirizano wa Akhristu Umalemekeza Mulungu

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 20, 25

November 15-21, 2010

“Mtsogoleri Wanu ndi Mmodzi, Khristu”

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 5, 25

November 22-28, 2010

Mtsogoleri Wathu Akuchita Zambiri Masiku Ano

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 6, 44

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 MASAMBA 7-11

Atumiki a Mulungu amafuna madalitso a Yehova kuti akwanitse kutsatira mfundo zake zolungama. Koma kodi n’chiyani chimene ayenera kuyesetsa kuchita? Kodi mzimu woyera wa Yehova ungatithandize bwanji kulimbana ndi mavuto alionse amene timakumana nawo?

NKHANI ZOPHUNZIRA 2, 3 MASAMBA 12-20

Nkhani ziwirizi zisonyeza kuti zimakhala zabwino ndiponso zosangalatsa ngati abale akukhala limodzi mogwirizana. Tionanso mfundo zotsimikizira kuti ndi Yehova yekha amene angagwirizanitse mitundu yonse ya anthu. Kenako tikambirana zimene aliyense payekha angachite polimbikitsa mgwirizano mumpingo chifukwa izi zimalemekeza Mulungu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 MASAMBA 21-29

Nkhani ziwirizi zitithandiza kudziwa bwino Khristu monga Mfumu kumwamba ndiponso Wolamulira wathu amene akuchita zambiri masiku ano. Iye amaona bwinobwino zimene zikuchitika m’mipingo ya ophunzira ake masiku ano.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Kutumikira pa Nthawi Imene Ntchito Yolalikira Yapita Patsogolo Kwambiri 3

Ntchito Yapadera ku Bulgaria Inali ndi Zotsatira Zabwino 30

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena