Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 2/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2011
w11 2/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

April 4-10, 2011

Mzimu Woyera Unagwira Ntchito Polenga Zinthu

TSAMBA 6

NYIMBO ZOIMBA: 15, 2

April 11-17, 2011

Anthu Ovomerezeka ndi Mulungu Adzapeza Moyo Wosatha

TSAMBA 13

NYIMBO ZOIMBA: 27, 51

April 18-24, 2011

Muzikonda Chilungamo ndi Mtima Wanu Wonse

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 22, 40

April 25, 2011–May 1, 2011

Kodi Mumadana ndi Kusamvera Malamulo?

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 29, 6

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 6-10

Mfundo za m’nkhani ino zitithandiza kumvetsa bwino mmene Mulungu anagwiritsira ntchito mzimu woyera polenga kumwamba ndi dziko lapansi. Nkhani imeneyi itithandizanso kulimbitsa chikhulupiriro chathu kuti Yehova ndi Mlengi wanzeru ndiponso wamphamvu.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 13-17

Nthawi zambiri anthu amadera nkhawa zinthu zakuthupi. Koma Baibulo limasonyeza kuti tiyenera kumaganizira kwambiri za kukhala wovomerezeka ndi Mulungu. Nkhaniyi ifotokoza bwino kufunika kokhulupirira kwambiri Yehova ndipo isonyezanso zimene tingachite kuti tikhale ovomerezeka ndi iye.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 24-32

‘Yesu ankakonda chilungamo ndipo ankadana ndi kusamvera malamulo.’ (Aheb. 1:9) Nkhanizi zitiuza mmene tingamutsanzirire. Zifotokoza bwino kufunika kokonda chilungamo ndiponso kudana ndi kusamvera malamulo.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

3 Phunzitsani Ana Anu Ulemu

11 Kodi Tiyeneradi Kuchita Khama?

12 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

18 Kodi Mumayamikiradi Madalitso Amene Mwalandira?

21 “Kumvera Kuposa Nsembe”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena