Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 12/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2011
w11 12/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

January 30, 2012–February 5, 2012

Kodi Solomo Ndi Chitsanzo Chabwino Kapena Choipa?

TSAMBA 8

NYIMBO ZOIMBA: 61, 57

February 6-12, 2012

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kutsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu?

TSAMBA 13

NYIMBO ZOIMBA: 71, 63

February 13-19, 2012

Anthu Okhulupirika Akale Amene Anatsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu

TSAMBA 18

NYIMBO ZOIMBA: 81, 51

February 20-26, 2012

Mzimu wa Mulungu Unkatsogolera Akhristu Oyambirira Ndipo Ukutsogoleranso Akhristu Masiku Ano

TSAMBA 22

NYIMBO ZOIMBA: 69, 122

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 8-12

Anthu ena otchulidwa m’Baibulo anapereka chitsanzo chabwino koma anachita zinthu zinanso zimene tiyenera kupewa. Nkhani ino itithandiza kuona zinthu zabwino komanso zoipa zimene Solomo anachita. Tiyeni tione zimene iye anachita n’cholinga choti tizichita bwino pa moyo wathu monga Akhristu.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 13-17

M’chilengedwechi muli mphamvu ina imene ingathe kutitsogolera bwinobwino m’dziko loipali. Kodi mphamvu imeneyi ndi iti ndipo n’chifukwa chiyani iyenera kutitsogolera? Kodi tingatani kuti izitithandiza kwambiri pa moyo wathu?

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 18-26

Atumiki a Mulungu ambiri a m’mbuyomu anapatsidwa mzimu woyera. Kodi mzimuwo unkawathandiza bwanji? Kuona mmene Yehova ankawathandizira kungatilimbikitse kwambiri pamene tikuchita utumiki wathu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Ndapindula Kwambiri Chifukwa Chololera Kusintha Zinthu

27 Musalole Kuti Matenda Akulandeni Chimwemwe

31 Kodi Mukukumbukira?

32 Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2011

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena