Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

APRIL 30, 2012–MAY 6, 2012

Thandizani Anthu Kuti ‘Adzuke ku Tulo’

TSAMBA 10 • NYIMBO: 65, 96

MAY 7-13, 2012

Khalanibe Odzipereka

TSAMBA 15 • NYIMBO: 92, 47

MAY 14-20, 2012

Tizisangalala ndi Chiyembekezo Chathu

TSAMBA 20 • NYIMBO: 129, 134

MAY 21-27, 2012

Musamayang’ane “Zinthu za M’mbuyo”

TSAMBA 25 • NYIMBO: 119, 17

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 10-19

Ziphunzitso zonyenga zachititsa kuti anthu ambiri akhale m’tulo tauzimu. Nkhani ziwirizi zikufotokoza mmene tingadzutsire anthu komanso chifukwa chake tiyenera kuchita zimenezi mwachangu. Ikufotokozanso tanthauzo la kulalikira modzipereka komanso zimene tingachite kuti ifeyo tikhale maso.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 20-24

Mtumwi Petulo analemba kuti Akhristu odzozedwa ali ndi “chiyembekezo cha moyo.” (1 Pet. 1:3) Kodi zimenezi zikutanthauza chiyani ndipo zikukhudza bwanji a “nkhosa zina”? (Yoh. 10:16) Nkhaniyi ikuthandizani kuona chifukwa chake muyenera kusangalala ndi chiyembekezo chanucho komanso kuyembekezera mwachidwi kukwaniritsidwa kwake.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 TSAMBA 25-29

Yesu anachenjeza kuti: “Kumbukirani mkazi wa Loti.” (Luka 17:32) Kodi pamenepa Yesu ankatanthauza chiyani? Nkhaniyi ifotokoza mbali zitatu zimene tiyenera kutsatira chenjezo limeneli. Mwinatu pa mbali zimenezi pali mbali imodzi kapena zingapo zimene muyenera kusintha kuti mutsatire bwinobwino chenjezoli.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 “Kudzanja Lanu Lamanja Kuli Chimwemwe Mpaka Muyaya”

7 Kodi Mumatani Ena Akakupemphani Malangizo?

30 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

32 “Kodi Mungatijambule?”

PATSAMBA LOYAMBA: Achinyamata ambiri ku Malawi amalalikira kwa anzawo kusukulu ndipo amawafotokozera mfundo zosangalatsa ndiponso zofunika kwambiri za m’buku lakuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa

MALAWI

KULI ANTHU OKWANA

13,077,160

KULI OFALITSA OKWANA

79,157

NYUMBA ZA UFUMU ZIMENE ZAMANGIDWA

1,031 kuyambira mu 1998

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena