Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

MAY 28, 2012–JUNE 3, 2012

‘Mwana Amakonda Kuululira Ena za Atate’

TSAMBA 3 • NYIMBO: 106, 112

JUNE 4-10, 2012

Kusakhulupirika Ndi Chizindikiro cha Masiku Otsiriza

TSAMBA 8 • NYIMBO: 63, 32

JUNE 11-17, 2012

Pitirizani Kutumikira Yehova ndi Mtima Wathunthu

TSAMBA 13 • NYIMBO: 52, 57

JUNE 18-24, 2012

Yehova Amadziwa Kupulumutsa Anthu Ake

TSAMBA 22 • NYIMBO: 133, 131

JUNE 25, 2012–JULY 1, 2012

Yehova Amatiteteza Kuti Tidzapulumuke

TSAMBA 27 • NYIMBO: 110, 60

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 3-7

Kodi Yesu anaulula za Atate kwa ophunzira ake ndiponso ena m’njira ziwiri ziti? Nanga tingatsanzire bwanji Yesu poululira ena za Atate wake? Nkhani iyi idzatithandiza kuyankha mafunsowa.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 8-12

Kusakhulupirika kwafala kwambiri m’dzikoli. Koma tisalole kuti kusakhulupirikako kusokoneze mtendere ndiponso mgwirizano zimene Akhristufe tili nazo m’banja komanso mu mpingo. Nkhani iyi ikusonyeza kuti tingapitirize kukhala okhulupirika kwa Mulungu ndiponso kwa anzathu.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 13-17

Kodi timasonyeza bwanji kuti tikutumikira Yehova ndi mtima wathunthu? Kodi tiyenera kuteteza mtima wathu ku chinthu choopsa chiti? N’chiyani chingatithandize kupitiriza kutumikira Yehova ndi mtima wathunthu? Mayankho a mafunsowa ali m’nkhani imeneyi.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 TSAMBA 22-31

Pa “chisautso chachikulu” anthu a Mulungu adzaukiridwa moopsa. (Mat. 24:21) Kodi tikudziwa bwanji kuti Yehova adzatipulumutsa? Kodi amatithandiza bwanji kuti tipitirize kukhala okhulupirika n’kumayembekeza mapeto a dzikoli? Mudzapeza mayankho olimbitsa chikhulupiriro m’nkhani zimenezi.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

18 Ndagwira Chovala cha Myuda kwa Zaka Zoposa 70

32 Kodi Mukukumbukira?

PATSAMBA LOYAMBA: Mlongo akupereka kabuku ka chinenero cha Inuktitut ali kudera la chipale chofewa ku Frobisher Bay mumzinda wa Iqaluit kuchigawo cha Nunavut m’dziko la Canada

CANADA

KULI ANTHU OKWANA

34,017,00

KULI OFALITSA OKWANA

113,989

NTCHITO YOMASULIRA MABUKU

Nthambi ya ku Canada imayang’anira ntchito yomasulira mabuku m’zinenero 12 za kumeneko

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena