Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

FEBRUARY 25, 2013–MARCH 3, 2013

Ukhale Wolimba Mtima Chifukwa Yehova Ali Nawe

TSAMBA 7 • NYIMBO: 60, 23

MARCH 4-10, 2013

Musalole Chilichonse Kusokoneza Ubwenzi Wanu ndi Yehova

TSAMBA 12 • NYIMBO: 106, 51

MARCH 11-17, 2013

Pitirizani Kuyandikira Yehova

TSAMBA 17 • NYIMBO: 52, 65

MARCH 18-24, 2013

Tumikirani Yehova Popanda Kunong’oneza Bondo

TSAMBA 22 • NYIMBO: 91, 39

MARCH 25-31, 2013

Akulu Achikhristu Ndi Antchito Anzathu Otipatsa Chimwemwe

TSAMBA 27 • NYIMBO: 123, 53

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Ukhale Wolimba Mtima Chifukwa Yehova Ali Nawe

Anthu ambiri a m’Baibulo anasonyeza chikhulupiriro ndiponso kulimba mtima. Kuganizira zitsanzo zawo kungatithandize kukhala ndi chikhulupiriro ndiponso kutumikira Yehova molimba mtima. Nkhaniyi ikufotokoza za lemba lathu la chaka cha 2013.

▪ Musalole Chilichonse Kusokoneza Ubwenzi Wanu ndi Yehova

▪ Pitirizani Kuyandikira Yehova

Pali zinthu zambiri pa moyo zomwe sitingathe kusankha. Mwachitsanzo, sitingathe kusankha makolo athu, abale athu kapena kumene tingabadwire. Koma n’zosiyana pa nkhani ya ubwenzi wathu ndi Yehova. Tikhoza kusankha kumuyandikira kapena ayi. Nkhanizi zikufotokoza zinthu 7 zimene zikhoza kusokoneza ubwenzi wathu ndi Yehova.

▪ Tumikirani Yehova Popanda Kunong’oneza Bondo

Tonsefe tachita zinthu zina zimene timanong’oneza nazo bondo. Koma tisalole zimenezi kutisokoneza potumikira Mulungu. M’nkhaniyi, tiphunzira mmene tingatsatirire chitsanzo cha mtumwi Paulo popitiriza kutumikira Yehova popanda kunong’oneza bondo.

▪ Akulu Achikhristu Ndi Antchito Anzathu Otipatsa Chimwemwe

M’kalata yake yachiwiri yopita kwa Akorinto, Paulo anafotokoza kuti iye ndi anzake apamtima anali ‘antchito anzawo kuti akhale ndi chimwemwe.’ (2 Akor. 1:24) Kodi mawu a Paulo amenewa angathandize bwanji akulu achikhristu? Kodi aliyense wa ife angathandize bwanji kuti anthu mu mpingo akhale achimwemwe? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Norway

32 Anabala Zipatso Chifukwa Chokonzekera Bwino

TSAMBA LOYAMBA: Banja lina limene linapuma pa ntchito likuchititsa phunziro la Baibulo pakhonde la nyumba ina mumzinda wa Camp Perrin. Anthu ena a ku Haiti amene anali kukhala kudziko lina, ngati banjali, abwerera kwawo ku Haiti kuti atumikire kumene kulibe ofalitsa okwanira

HAITI

WOFALITSA ALIYENSE KU HAITI AYENERA KULALIKIRA ANTHU

557

KULI OFALITSA

17,954

MAPHUNZIRO A BAIBULO

35,735

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena