Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

MARCH 3-9, 2014

Lambirani Yehova, Mfumu Yamuyaya

TSAMBA 7 • NYIMBO: 106, 46

MARCH 10-16, 2014

Kodi Ufumu Umene Walamulira kwa Zaka 100 Umakukhudzani Bwanji?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 97, 101

MARCH 17-23, 2014

Achinyamata, Muzisankha Zochita Mwanzeru

TSAMBA 17 • NYIMBO: 41, 89

MARCH 24-30, 2014

Tumikirani Yehova Masiku Oipa Asanafike

TSAMBA 22 • NYIMBO: 54, 17

MARCH 31, 2014–APRIL 6, 2014

Kodi Ufumu wa Mulungu Ubwera Liti?

TSAMBA 27 • NYIMBO: 108, 30

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Lambirani Yehova, Mfumu Yamuyaya

Nkhaniyi ititsimikizira kuti Yehova wakhala Mfumu kuyambira kale. Itithandiza kudziwa mmene Yehova wasonyezera kuti ndi Mfumu kwa angelo ndiponso anthu. Itilimbikitsanso kutsatira zitsanzo za anthu akale amene anasankha kulambira Yehova, yemwe ndi Mfumu yamuyaya.

▪ Kodi Ufumu Umene Walamulira kwa Zaka 100 Umakukhudzani Bwanji?

Nkhaniyi itithandiza kumvetsa bwino zimene Ufumu wa Mesiya wachita pa zaka 100 zoyambirira zimene wakhala ukulamulira. Itilimbikitsanso kugonjera mokhulupirika Ufumuwu komanso itithandiza kuganizira kwambiri tanthauzo la lemba lathu la chaka cha 2014.

▪ Achinyamata, Muzisankha Zochita Mwanzeru

▪ Tumikirani Yehova Masiku Oipa Asanafike

Kodi ndidzachita chiyani pa moyo wanga? Munthu aliyense amene wadzipereka kwa Yehova ayenera kudzifunsa funsoli. Nkhanizi zikufotokoza mfundo zimene zingathandize Akhristu achinyamata kuchita zambiri potumikira Mulungu. Ikusonyezanso kuti Akhristu achikulire ali ndi mwayi wochita zambiri mu utumiki.

▪ Kodi Ufumu wa Mulungu Ubwera Liti?

Masiku ano, anthu ambiri amasokonezedwa ndi zinthu zimene zikuchitika m’dzikoli kapena ndi zinthu zimene iwowo akuchita. Nkhaniyi ikufotokoza zifukwa zitatu zotsimikizira Akhristu kuti posachedwapa Ufumu wa Mulungu uwononga dziko loipali.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse Kumadzulo kwa Africa

32 Zimene Ndinasankha Ndili Mwana

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira anthu ochokera kumayiko ena amene akuphunzira payunivesite ina mumzinda wa Lviv

UKRAINE

KULI ANTHU OKWANA

45,561,000

KULI OFALITSA OKWANA

150,887

Kuli mipingo 1,737 ndiponso magulu 373 mu zinenero 15. Zinenerozi zikuphatikizapo Chihangare, Chiromaniya, Chirasha, chinenero chamanja cha Chirasha ndiponso Chiyukireniya

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena