Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

MAY 5-11, 2014

Kodi Tingatani Kuti Tikhalebe ndi Mtima Wodzipereka?

TSAMBA 7 • NYIMBO: 61, 25

MAY 12-18, 2014

Kodi Tingatani Kuti Tikhalebe Osangalala?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 74, 119

MAY 19-25, 2014

Muzilemekeza Anthu Achikulire

TSAMBA 20 • NYIMBO: 90, 135

MAY 26, 2014–JUNE 1, 2014

Kodi Achikulire Tingawasamalire Bwanji?

TSAMBA 25 • NYIMBO: 134, 29

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Kodi Tingatani Kuti Tikhalebe ndi Mtima Wodzipereka?

Tili ndi mdani wochenjera amene safuna kuti tizitumikira Mulungu modzipereka. Nkhaniyi itithandiza kudziwa mdani ameneyu komanso mmene tingagwiritsire ntchito Baibulo polimbana naye.

▪ Kodi Tingatani Kuti Tikhalebe Osangalala?

Kukhalabe wosangalala kungatithandize kupirira pamene tikulambira Yehova. N’chifukwa chiyani anthu ena amadziona kuti ndi achabechabe? Nkhaniyi itisonyeza mmene Baibulo lingatithandizire kuti tikhalebe osangalala.

▪ Muzilemekeza Anthu Achikulire

▪ Kodi Achikulire Tingawasamalire Bwanji?

Nkhanizi zikufotokoza udindo umene Mkhristu aliyense komanso mpingo uli nawo posamalira Akhristu anzathu kapena achibale okalamba. Tionanso zimene tingachite kuti tikwanitse udindo umenewu.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi Tingathandize Bwanji Achibale Omwe Si Mboni?

17 Kulambira kwa Pabanja Kuzikhala Kosangalatsa

30 Mawu Anu “Asakhale Inde Kenako Ayi”

PATSAMBA LOYAMBA: Abale ndi alongo ena ku Australia amayenda mtunda wautali kuti akalalikire kwa alimi a ng’ombe

AUSTRALIA

KULI ANTHU OKWANA

23,192,500

KULI OFALITSA OKWANA

66,967

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena