Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 8/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 8/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

SEPTEMBER 29, 2014–OCTOBER 5, 2014

Akazi Amathandiza Pokwaniritsa Cholinga cha Yehova

TSAMBA 6 • NYIMBO: 86, 104

OCTOBER 6-12, 2014

Muzigwiritsa Ntchito Mawu a Mulungu Chifukwa Ndi Amoyo

TSAMBA 11• NYIMBO: 114, 101

OCTOBER 13-19, 2014

Zimene Yehova Wachita Kuti Tiyandikane Naye

TSAMBA 16 • NYIMBO: 51, 91

OCTOBER 20-26, 2014

Muzimva Mawu a Yehova Nthawi Zonse

TSAMBA 21 • NYIMBO: 26, 89

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Akazi Amathandiza Pokwaniritsa Cholinga cha Yehova

M’nkhaniyi muona kuti zimene zinachitika m’Munda wa Edeni zakhudza amuna ndi akazi onse. Muonanso zimene akazi oopa Mulungu akale anakumana nazo. Komanso muona zimene akazi achikhristu masiku ano amachita pokwaniritsa cholinga cha Mulungu.

▪ Muzigwiritsa Ntchito Mawu a Mulungu Chifukwa Ndi Amoyo

Wofalitsa aliyense amafunitsitsa kuti aziphunzitsa mogwira mtima mu utumiki. Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zina zomwe zingatithandize kugwiritsa ntchito Baibulo ndiponso timapepala pokambirana ndi anthu. Tikatero tiziwafika pamtima ndi Mawu a Yehova, omwe ndi amoyo.

▪ Zimene Yehova Wachita Kuti Tiyandikane Naye

Timafunikira kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Mlengi wathu. Nkhaniyi ikusonyeza kuti Yehova wapereka dipo komanso Mawu ake chifukwa chofunitsitsa kuti tikhale naye pa ubwenzi wabwino.

▪ Muzimva Mawu a Yehova Nthawi Zonse

Tiyenera kumvetsera mawu a Yehova kuti tiziyenda m’njira ya choonadi. M’nkhaniyi tiphunzira zimene tingachite kuti tizimvetsera mawu a Yehova ngakhale kuti Satana akuyesetsa kutisokoneza komanso tikulimbana ndi zilakolako zoipa. Nkhaniyi itithandizanso kudziwa kuti kupemphera kwa Mulungu woona n’kofunika kwambiri.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi Mukulandira “Chakudya pa Nthawi Yoyenera?”

26 ‘Ubwerere Ukalimbikitse Abale Ako’

29 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Alongo akulalikira mu Chirasha m’mphepete mwa nyanja mumzinda wa Tel-Aviv. Kumbuyo kwawo kuli mapiri a m’dera la Jaffa kumene kunali doko lakale la Yopa

ISRAEL

KULI ANTHU

8,050,000

CHIWERENGERO CHAPAMWAMBA CHA OFALITSA MU 2013

1,459

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2013

2,671

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena