Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

OCTOBER 27, 2014–NOVEMBER 2, 2014

N’chiyani Chimakutsimikizirani Kuti Muli M’gulu la Yehova?

TSAMBA 7 • NYIMBO: 28, 107

NOVEMBER 3-9, 2014

Tumikirani Mulungu Mokhulupirika Pokumana ndi “Masautso Ambiri”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 135, 133

NOVEMBER 10-16, 2014

Makolo, Muzisamalira Bwino Ana Anu

TSAMBA 17 • NYIMBO: 88, 24

NOVEMBER 17-23, 2014

Mdani Wathu Womalizira Adzawonongedwa

TSAMBA 23 • NYIMBO: 111, 109

NOVEMBER 24-30, 2014

Muzikumbukira Atumiki a Nthawi Zonse

TSAMBA 28 • NYIMBO: 95, 100

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ N’chiyani Chimakutsimikizirani Kuti Muli M’gulu la Yehova?

Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zimene zimachititsa anthu ambiri kutsimikizira kuti Mboni za Yehova ndi Akhristu enieni. Tionanso zimene zimachititsa abale ndi alongo ena kutsimikizira kuti alidi m’gulu la Yehova.

▪ Tumikirani Mulungu Mokhulupirika Pokumana ndi “Masautso Ambiri”

M’dziko la Satanali timakumana ndi masautso ambiri. Masautso ena amabwera chifukwa cha kuzunzidwa koma ena ndi ovuta kuwazindikira. Nkhaniyi itithandiza kuzindikira masautsowa komanso kukonzekera misampha ya Satana.

▪ Makolo, Muzisamalira Bwino Ana Anu

Makolo ayenera kulera ana awo “m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake.” (Aef. 6:4) Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zitatu zimene angachite kuti azisamalira bwino ana awo.

▪ Mdani Wathu Womalizira Adzawonongedwa

Kodi imfa inayamba bwanji? Nanga mdani ameneyu adzawonongedwa bwanji? (1 Akor. 15:26) Nkhaniyi ikuyankha mafunso amenewa ndipo ikusonyeza kuti Yehova ndi wachilungamo, wanzeru komanso wachikondi.

▪ Muzikumbukira Atumiki a Nthawi Zonse

Pali anthu ambiri amene akhala akuchita utumiki wa nthawi zonse ngakhale kuti amakumana ndi mavuto m’dziko loipali. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timakumbukira ‘ntchito zawo zachikhulupiriro ndiponso zachikondi’?—1 Ates. 1:3.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi ‘Mukuyesetsa Kuti Mukhale Woyang’anira’?

22 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

PATSAMBA LOYAMBA: Abale awiri akulalikira msodzi m’mphepete mwa nyanja mumzinda wa Negombo ku Sri Lanka

SRI LANKA

KULI ANTHU

20,860,000

KULI OFALITSA

5,600

APAINIYA OKHAZIKIKA

641

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena