Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 12/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 12/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

FEBRUARY 2-8, 2015

‘Mverani Ndipo Mumvetse Tanthauzo Lake’

TSAMBA 6 • NYIMBO: 92, 120

FEBRUARY 9-15, 2015

Kodi Timamvetsa Tanthauzo Lake?

TSAMBA 11 • NYIMBO: 97, 96

FEBRUARY 16-22, 2015

Tizigwirizana Kwambiri Pamene Mapeto Akuyandikira

TSAMBA 22 • NYIMBO: 107, 29

FEBRUARY 23, 2015–MARCH 1, 2015

Kodi Mumayamikira Zimene Muli Nazo?

TSAMBA 27 • NYIMBO: 89, 135

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ ‘Mverani Ndipo Mumvetse Tanthauzo Lake’

▪ Kodi Timamvetsa Tanthauzo Lake?

Kodi tingatani kuti timvetse bwino mafanizo a Yesu? Nkhani ziwirizi zitithandiza kumvetsetsa mafanizo 7 a Yesu. Zitithandizanso kudziwa mmene tingagwiritsire ntchito zimene taphunzira pa mafanizowa pokambirana ndi anthu mu utumiki.

▪ Tizigwirizana Kwambiri Pamene Mapeto Akuyandikira

▪ Kodi Mumayamikira Zimene Muli Nazo?

M’dzikoli achinyamata ambiri ndi odzikonda. Koma achinyamata achikhristu ayenera kugwirizana kwambiri ndi gulu la Yehova. Nkhanizi zikufotokoza zitsanzo zabwino ndiponso zoipa. Zikufotokozanso mfundo zimene zingathandize achinyamata komanso achikulire kuti azisankha bwino zochita.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 ‘Ankadziwa Njira Yake’

4 Yehova Amadalitsa Anthu Opereka ndi Mtima Wonse

16 Kodi Mukukumbukira?

17 Kodi Ndi Bwino Kusintha Maganizo Anu?

21 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

32 Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2014

PATSAMBA LOYAMBA: Anthu ena amene amapita ku Tamarindo m’mphepete mwa nyanja ya Pacific m’dziko la Costa Rica amasangalala kuphunzira kuti m’tsogolo dziko lonse lidzakhala paradaiso

COSTA RICA

KULI OFALITSA

29,185

KULI APAINIYA

2,858

Dzina la Mulungu lakuti Yehova,

Jéoba

mu chilankhulo cha Chibiribiri

Jehová

mu chilankhulo cha Chikabeka

Kuli mipingo iwiri ndiponso timagulu tiwiri mu chilankhulo cha Chibiribiri ndipo kuli mipingo itatu ndiponso timagulu 4 mu Chikabeka

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena