Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IYI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

MARCH 2-8, 2015

Yamikani Yehova Ndipo Adzakudalitsani

TSAMBA 8 • NYIMBO: 2, 75

MARCH 9-15, 2015

N’chifukwa Chiyani Timachita Mwambo Wokumbukira Imfa ya Yesu?

TSAMBA 13 • NYIMBO: 8, 109

MARCH 16-22, 2015

Limbitsani Banja Lanu Kuti Likhale Losangalala

TSAMBA 18 • NYIMBO: 36, 51

MARCH 23-29, 2015

Lolani Kuti Yehova Alimbitse Ndiponso Kuteteza Banja Lanu

TSAMBA 23 • NYIMBO: 87, 50

MARCH 30, 2015–APRIL 5, 2015

Kodi N’zotheka Kukondana Mpaka Kalekale?

TSAMBA 28 • NYIMBO: 72, 63

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Yamikani Yehova Ndipo Adzakudalitsani

Kuti tikhalebe ndi mtima woyamikira, tiyenera kuganizira madalitso amene Yehova watipatsa ndiponso kumuthokoza. Mtimawu ukhoza kutisiyanitsa ndi anthu osayamika komanso ungatithandize kuti tipirire mavuto. Lemba la chaka cha 2015 litithandiza kuti tizikumbukira kuyamika Yehova.

▪ N’chifukwa Chiyani Timachita Mwambo Wokumbukira Imfa ya Yesu?

Nkhaniyi ikufotokoza bwino chifukwa chimene timachitira mwambo wokumbukira imfa ya Yesu. Kodi mkate ndi vinyo zimaimira chiyani? Kodi munthu angadziwe bwanji kuti ndi woyenera kudya mkate ndiponso kumwa vinyo? Nanga tingakonzekere bwanji mwambowu? Nkhaniyi iyankha mafunso onsewa.

▪ Limbitsani Banja Lanu Kuti Likhale Losangalala

▪ Lolani Kuti Yehova Alimbitse Ndiponso Kuteteza Banja Lanu

Mabanja ambiri akukumana ndi mavuto komanso amayesedwa. Koma Yehova akhoza kuthandiza anthu kukhala ndi banja lolimba komanso losangalala. Nkhani yoyamba ikufotokoza zinthu 5 zimene zingathandize kuti banja likhale lolimba komanso losangalala ndipo ikusonyeza kuti chikondi n’chofunika kwambiri m’banja. Nkhani yachiwiri ikusonyeza zimene mwamuna ndi mkazi angachite kuti ubwenzi wawo m’banja komanso ndi Yehova ukhale wolimba.

▪ Kodi N’zotheka Kukondana Mpaka Kalekale?

Kodi mungafotokoze bwanji chikondi chenicheni chimene chimakhala pakati pa mwamuna ndi mkazi? Kodi n’zotheka kukondana mpaka kalekale? Kodi anthu angasonyezane bwanji chikondichi? Nkhaniyi ikufotokoza chikondi chenicheni ndipo yachokera m’buku la Nyimbo ya Solomo.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IYI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku New York

PATSAMBA LOYAMBA: Akugwiritsa ntchito Baibulo polalikira ku Grindelwald, ndipo mapiri okongola akuoneka chapafupi

SWITZERLAND

KULI ANTHU

7,876,000

KULI OFALITSA

18,646

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO (2013)

31,980

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena