Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IYI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

OCTOBER 26, 2015–NOVEMBER 1, 2015

Kodi Mukuyesetsa Kukhala Ngati Khristu?

TSAMBA 3

NOVEMBER 2-8, 2015

Kodi Chikumbumtima Chanu Chimakuthandizani Kusankha Zochita Mwanzeru?

TSAMBA 8

NOVEMBER 9-15, 2015

Khalani ndi Chikhulupiriro Cholimba

TSAMBA 13

NOVEMBER 16-22, 2015

Kodi Yehova Amasonyeza Bwanji Kuti Amatikonda?

TSAMBA 18

NOVEMBER 23-29, 2015

Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Timakonda Yehova?

TSAMBA 23

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Kodi Mukuyesetsa Kukhala Ngati Khristu?

▪ Kodi Chikumbumtima Chanu Chimakuthandizani Kusankha Zochita Mwanzeru?

M’nkhanizi tiona zimene tingachite polimbitsa ubwenzi wathu ndi Mulungu n’cholinga choti tikhale Akhristu olimba. Tionanso zimene tingachite pophunzitsa chikumbumtima chathu kuti chizititsogolera bwino posankha zochita.

▪ Khalani ndi Chikhulupiriro Cholimba

Tsiku lina Petulo anayesa kuyenda panyanja ya Galileya koma chikhulupiriro chake chitachepa anayamba kumira. M’nkhaniyi tiona zinthu zimene zingatithandize kudziwa ngati chikhulupiriro chathu chayamba kuchepa komanso zimene tingachite kuti tichilimbitse.

▪ Kodi Yehova Amasonyeza Bwanji Kuti Amatikonda?

▪ Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Timakonda Yehova?

Tikadziwa zoti Yehova amatikonda ndipo nafenso n’kumamukonda, timasangalala kwambiri. Nkhani ziwirizi zikusonyeza umboni wakuti Yehova amatikonda komanso zimene tingachite posonyeza kuti timamukonda.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IYI

28 Madalitso a Yehova Andilemeretsa

PATSAMBA LOYAMBA: Abale ndi alongo a ku Italy amene ali mumpingo wachitchainizi akulalikira kwa anthu obwera mumzinda wa Rome. Abale ndi alongowa amaika mashelefu a matayala pafupi ndi nyumba zakale zotchuka ndipo anthu ambiri amabwera kudzatenga mabuku

ITALY

KULI ANTHU

60,782,668

KULI OFALITSA

251,650

KULI APAINIYA

33,073

Abale ndi alongo oposa 24,000 amalalikira m’zilankhulo zakunja zokwana 37

Chithunzi patsamba 2
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena