Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 October tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 October tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Mbiri ya Moyo Wanga-Ndimayesetsa Kutengera Anthu a Zitsanzo Zabwino

MLUNGU WA NOVEMBER 28, 2016–DECEMBER 4, 2016

8 “Musaiwale Kuchereza Alendo”

MLUNGU WA DECEMBER 5-11, 2016

13 Mungatani Kuti Mukhalebe Olimba Mwauzimu mu Mpingo wa Chilankhulo China?

Masiku ano m’mipingo yambiri mukumapezeka anthu a chilankhulo china kapena ochokera m’mayiko ena. Nkhani yoyamba ikufotokoza mmene tingathandizire anthu oterewa amene timasonkhana nawo mu mpingo wathu. Nkhani yachiwiri ikufotokoza zimene Akhristu ochokera m’mayiko ena angachite kuti akhalebe olimba mwauzimu.

18 Kodi ‘Mumasunga Nzeru Zopindulitsa’?

MLUNGU WA DECEMBER 12-18, 2016

21 Muzikhulupirira Kwambiri Zinthu Zimene Mukuyembekezera

MLUNGU WA DECEMBER 19-25, 2016

26 Muzisonyeza Kuti Mumakhulupirira Malonjezo a Yehova

Nkhanizi zikufotokoza tanthauzo la chikhulupiriro limene lafotokozedwa pa Aheberi 11:1. Nkhani yoyamba ikufotokoza zimene tingachite kuti tikhale ndi chikhulupiriro cholimba. Nkhani yachiwiri ikusonyeza kuti kukhala ndi chikhulupiriro sikumangotanthauza kumvetsa malonjezo a Mulungu.

31 Kodi Mukudziwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena