Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 November tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 November tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Mawu Olimbikitsa Kwambiri

MLUNGU WA DECEMBER 26, 2016–JANUARY 1, 2017

4 Tipitirize Kulimbikitsana Tsiku ndi Tsiku

Yehova Mulungu ndi Yesu Khristu amapereka chitsanzo chabwino kwambiri pa nkhani yolimbikitsa ena. Mtumwi Paulo ankaonanso kuti kulimbikitsana n’kofunika kwambiri. Chitsanzo chawo chingatithandize kuti tizikondana komanso kulimbikitsana kunyumba kwathu komanso ku Nyumba ya Ufumu.

MLUNGU WA JANUARY 2-8, 2017

9 Mawu a Mulungu Amatithandiza Kuti Tizichita Zinthu Mwadongosolo

MLUNGU WA JANUARY 9-15, 2017

14 Kodi Mumaona Kuti Baibulo Ndi Buku Lapadera?

M’nkhanizi tipeza mayankho a mafunso awa: N’chiyani chimathandiza anthu Yehova kuti azichita zinthu mwadongosolo? Kodi tingatani kuti Mawu a Mulungu azitithandiza kuti tizichita zinthu mogwirizana? Nanga tingasonyeze bwanji kuti ndife okhulupirika kwa Yehova ndipo timathandiza gulu lake?

19 “Ntchitoyi Ndi Yaikulu”

MLUNGU WA JANUARY 16-22, 2017

21 Anthu a Mulungu Anaitanidwa Kuchoka mu Mdima

MLUNGU WA JANUARY 23-29, 2017

26 Anatuluka mu Babulo Wamkulu

Nkhani ziwirizi zikufotokoza nthawi imene anthu a Mulungu anali mu ukapolo wa Babulo wamkulu. Ikufotokozanso zimene odzozedwa anachita cha m’ma 1800 n’cholinga choti amvetse bwino Mawu a Yehova. Tikambirananso zimene Ophunzira Baibulo anachita kuti atuluke mu Babulo Wamkulu. Tionanso nthawi imene ukapolowo unatha.

31 Kale Lathu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena