Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 November tsamba 1-2
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 November tsamba 1-2
Nsanja ya Olonda Yophunzira, November 2016

Magazini Yophunzira

November 2016

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA DECEMBER 26, 2016 MPAKA JANUARY 29, 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PATSAMBA LOYAMBA:

ANGOLA

Apainiya apadera akuchititsa phunziro la Baibulo m’chinenero chamanja mumzinda wa Benguela pogwiritsa ntchito kabuku kakuti, Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha. Ofalitsa 10 amumzindawu, omwe ali ndi vuto losamva, anasangalala kwambiri pamene anthu okwana 62 anafika pa Chikumbutso mu 2015.

KULI OFALITSA

115,948

MAPHUNZIRO A BAIBULO

502,848

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO (2015)

529,827

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.

Ngati mukufuna kupereka pitani pawebusaiti yathu ya www.jw.org/ny.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena