Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 April tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 April tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA JUNE 4-10, 2018

3 Kodi Tingapeze Bwanji Ufulu Weniweni?

MLUNGU WA JUNE 11-17, 2018

8 Tizitumikira Yehova Mulungu Amene Amapereka Ufulu

Anthu ambiri masiku ano amamenyera ufulu wawo. Koma kodi Akhristu ayenera kukhala ndi maganizo otani pa nkhani ya ufulu? Nkhani ziwirizi zikufotokoza tanthauzo la ufulu weniweni komanso zimene tingachite kuti tiupeze. Zikusonyezanso mmene tingagwiritsire ntchito mwanzeru ufulu wathu kuti zinthu zitiyendere bwino komanso kuti tithandize anthu ena. Koma chofunika kwambiri n’chakuti tiona mmene tingagwiritsire ntchito ufulu wathu polemekeza Yehova amene amapereka ufulu weniweni.

13 Kodi Akulu ndi Atumiki Othandiza Angaphunzire Chiyani kwa Timoteyo?

MLUNGU WA JUNE 18-24, 2018

15 Tizitsanzira Yehova pa Nkhani Yolimbikitsa Ena

MLUNGU WA JUNE 25, 2018–JULY 1, 2018

20 Tizilimbikitsana Ndipo “Tiwonjezere Kuchita Zimenezi”

Nkhanizi zikusonyeza kuti Yehova wakhala akulimbikitsa atumiki ake ndipo atumiki akewo amamutsanzira n’kumalimbikitsana. Tionanso chifukwa chake tiyenera kulimbikitsana kwambiri masiku ano kuposa kale lonse

MLUNGU WA JULY 2-8, 2018

25 Achinyamata, Kodi Mukuyesetsa Kukwaniritsa Zolinga Zauzimu?

Achinyamata mumpingo zimawayendera bwino ngati ali ndi cholinga chosangalatsa Yehova. Nkhaniyi ikufotokoza chifukwa chake achinyamata ayenera kukhala ndi zolinga zauzimu adakali aang’ono. Ikufotokozanso ubwino woika patsogolo ntchito yolalikira.

30 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

32 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena