Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 May tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 May tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi

3 Mbiri ya Moyo Wanga​—Ndinali Wosauka Koma Panopa Ndine Wolemera

9 Mtendere, Kodi Mungaupeze Bwanji?

MLUNGU WA JULY 9-15, 2018

12 Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabereka Zipatso’ Mopirira

MLUNGU WA JULY 16-22, 2018

17 N’chifukwa Chiyani Tiyenera ‘Kupitiriza Kubala Zipatso Zambiri’?

Nkhani yoyamba ikufotokoza fanizo la Yesu lonena za mtengo wa mpesa komanso la wofesa mbewu ndipo ikusonyeza zimene tikuphunzira zokhudza ntchito yolalikira. Nkhani yachiwiri ikufotokoza zifukwa zingapo za m’Malemba zotichititsa kugwira ntchito yolalikira mopirira.

MLUNGU WA JULY 23-29, 2018

22 Kodi Mumamudziwa Bwino Mdani Wanu?

MLUNGU WA JULY 30, 2018–AUGUST 5, 2018

27 Achinyamata, Musasunthike Polimbana ndi Mdyerekezi

Satana ndi mdani wathu. Koma kodi ali ndi mphamvu zotani? Nanga kodi alibe mphamvu yochita zinthu ziti? Ndipo kodi n’chiyani chingatithandize tonsefe, kuphatikizapo achinyamata, kuti tilimbane naye? Nkhani ziwirizi ziyankha mafunso amenewa ndipo zitilimbikitsa kuti tikhale osasunthika polimbana ndi Mdyerekezi.

32 Zokolola N’zochuluka

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena