Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 5/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa May 11

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 11

Nyimbo Na. 117

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 19 ndime 1-8

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Eksodo 27–29

Na. 1: Eksodo 29:1-18

Na. 2: Mmene Tingakhalire Osangalala (lr-CN mutu 17)

Na. 3: Kukhulupirika Kolakwika Ndiponso Kuopsa Kwake

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 43

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Kodi Mungachite Upainiya Wothandiza M’miyezi Ikubwerayi? Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Gulu, masamba 112-113. Fotokozani zinthu zofunika kuti munthu ayenerere kuchita upainiya wothandiza ndipo pemphani amene anachitapo upainiya wothandiza m’mbuyomu kuti afotokoze madalitso amene anapeza.

Mph.10: Konzekerani ndi Banja Lanu Kuchita Nawo Utumiki. Mwachidule, funsani abale awiri omwe ndi mitu ya mabanja amene amapatula nthawi pamene akuchita Kulambira kwa Pabanja kuti akonzekere utumiki. Kodi amakonzekera bwanji, ndipo zimenezi zawathandiza motani? Banja limodzi lichite chitsanzo chosonyeza mmene amachitira pokonzekera kugawira magazini.

Mph.10: “Phunzitsani M’njira Yosavuta.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 158

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena