Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 18
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 18
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 5/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 18

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 18

Nyimbo Na. 24

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 19 ndime 9-17

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Eksodo 30–33

Na. 1: Eksodo 31:1-18

Na. 2: Chifukwa Chake Akhristu Oyambirira Anapatsidwa Mphatso za Kuchiritsa (rs-CN tsa. 169 ndime 1-4)

Na. 3: Kodi Mumakumbukira Kunena Kuti Zikomo? (lr-CN mutu 18)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 140

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Dzina la Mulungu Ndilo Linga Lolimba. Nkhani yochokera pa mfundo za pakamutu kachiwiri ka patsamba 274 m’buku la Sukulu ya Utumiki.

Mph.10: Zinthu Zitatu Zothandiza Kupeza Mawu Oyamba Abwino. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Kukambitsirana patsamba 9, ndime 1. Pomaliza kukambirana mfundozo, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambire kulankhula ndi anthu pogawira buku m’mwezi wa June.

Mph.10: “Kodi Tingakonzekere Bwanji Msonkhano wa Utumiki?” Nkhani yokambirana mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 28

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena