Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/09 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 5
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 9/09 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 5

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 5

Nyimbo Na. 173

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 27 ndime 1-7

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 1-3

Na. 1: Deuteronomo 2:1-15

Na. 2: Kodi Malemba a “M’Chipangano Chatsopano” Amasonyeza Kuti Anthu Adzalandira Moyo Wosatha Padziko Lapansi? (rs-CN tsa. 207 ndime 1–tsa. 208 ndime 1)

Na. 3: Kodi Ndani Adzauka kwa Akufa? Nanga Adzakhala Kuti? (lr-CN mutu 36)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 42

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10:  Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi? Nkhani yokambirana ndi omvera. Funsani omvera kuti afotokoze mafunso a m’kapepalaka amene anthu ambiri m’gawo lanu akufuna kudziwa mayankho ake. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritsirire ntchito kapepalaka kuti tiyambitse phunziro la Baibulo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Lalikirani Anthu Achinenero China. Nkhani yokambirana ndi omvera. Kambiranani mfundo zitatu zimene zili patsamba 2 m’kabuku kakuti Uthenga Wabwino wa Anthu a Mitundu Yonse. Ndipo pemphani wofalitsa kuti achite chitsanzo chosonyeza mmene mungagwiritsire ntchito kabukuka m’gawo lanu.

Nyimbo Na. 100

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena