Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/09 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 10/09 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa October 12

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 12

Nyimbo Na. 110

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 27, ndime 8 mpaka 15

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 4-6

Na. 1: Deuteronomo 4:15-28

Na. 2: Kukumbukira Yehova ndi Mwana Wake (lr-CN mutu 37)

Na. 3: Kodi Ndi Nthawi Iti Pamene Tinganene Kuti Zapang’ono Zipambana Zambiri? (Miy. 15:16)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 13

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kuchititsa Maphunziro a Baibulo a Panyumba. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 98, ndime 1 mpaka tsamba 99, ndime 1. Pemphani ofalitsa kuti afotokoze mwachidule chisangalalo chimene akhala nacho pophunzitsa wina choonadi.

Mph. 10: Buku Logawira mu October. Chitani zitsanzo ziwiri. Pa chitsanzo chimodzi mufunse funso limene lidzayankhidwe pa ulendo wobwereza. M’chitsanzo chinacho sonyezani mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo pa ulendo woyamba. Pambuyo pa chitsanzo chilichonse kambiranani mwachidule zimene tikuphunzira pa chitsanzocho.

Mph. 10: “Kodi Ndinu Wokonzeka Kuchita Ulaliki Wamwamwayi?” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 48

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena