Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 18
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 18
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 1/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 18

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 18

Nyimbo Na. 42

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 2, ndime 1-11

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 1-4

Na. 1: Oweruza 2:11-23

Na. 2: Kodi ndi Anthu Otani Amene Amapita ku Helo Wotchulidwa M’Baibulo? (rs tsa. 145 ndime 2 mpaka 4)

Na. 3: Mulungu Sanalenge Mdyerekezi

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 48

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Konzekerani Kugawira Magazini ya Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Fotokozani mwachidule mfundo za m’magaziniwa ndipo funsani omvera kuti atchule nkhani zimene akuona kuti zingachititse chidwi anthu m’gawo lanu. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa wamng’ono akukonzekera kugawira magazini.

Mph. 15: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana ndi omvera. Werengani malemba osagwidwa mawu ndipo kambiranani.

Nyimbo Na. 43

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena