Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 8/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa August 9

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 9

Nyimbo Na. 5

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 10 ndime 16 mpaka 24

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 21-22

Na. 1: 1 Mafumu 22:1-12

Na. 2: Kodi Munthu Akayamba Kuchita Nawo za M’dzikoli Chifukwa Chofuna Kudziimira Payekha, Amakhala Akulamuliridwa ndi Ndani? (rs tsa. 174 ndime 1-2)

Na. 3: Kodi Chitsanzo cha Eliya Chikutiphunzitsa Chiyani pa Nkhani ya Pemphero? (Yakobe 5:18)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 15

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Kodi Mfundo Yoti Zamoyo Zinachita Kusanduka Imagwirizanadi ndi Sayansi? Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 99 ndime 1 mpaka tsamba 104 ndime 1. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anagwiritsira ntchito mfundo zimenezi polalikira kusukulu kapena malo ena.

Mph. 15: “Mayi Wathanzi Amaberekanso Mwana Wathanzi.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Ikambidwe ndi mkulu woyenerera.

Nyimbo Na. 20

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena