Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/11 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 4

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 4
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 4
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 6/11 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa July 4

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 4

Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 9 ndime 10-16 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 60–68 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 62:1–63:5 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Tili Ndi Mbali Yotani pa Kukwaniritsidwa kwa Hagai 2:7? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Ndani Amene Ali Olamulira mu Ufumuwo?—rs tsa. 375 ndime 3 mpaka 5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 7

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Ngati Munthu Wanena Kuti: ‘Ndili Ndi Chipembedzo Changa.’ Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 18 ndime 2 mpaka tsamba 19 ndime 4. Pemphani omvera kuti anene njira zina zomwe aona kuti n’zothandiza poyankha anthu otero. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza mmene tingayankhire anthu pogwiritsa ntchito njira zimenezi.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Luka 9:57-62 ndi Luka 14:25-33. Kenako kambiranani mmene mavesiwa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Nyimbo Na. 50 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena