Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 7/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa July 11

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 11

Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 9 ndime 17-21 ndi bokosi patsamba 96 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 69–73 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 72:1-20 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Ufumu wa Mulungu Udzakhudza Bwanji Maboma a Anthu?—rs tsa. 376 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: Zimene Achinyamata Angaphunzire kwa Mfumu Hezekiya ndi Yosiya (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 20

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 30: “Masiku Atatu Otsitsimulidwa Mwauzimu.” Onani patsamba 3. Mafunso ndi mayankho. Kambiranani “Zofunika Kukumbukira pa Msonkhano Wachigawo.” Mukamakambirana ndime 5, funsani woyang’anira utumiki kuti afotokoze zimene zakonzedwa pa ntchito yogawira timapepala toitanira anthu kumsonkhano wachigawo.

Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena