Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/11 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 1
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 1
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 7/11 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa August 1

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 1

Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 10 ndime 18-23 ndi bokosi patsamba 107 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 87–91 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 89:26-52 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Zimene Zimachititsa Kuti Atumiki Okhulupirika a Yehova Azikhala Achimwemwe (Mph. 5)

Na. 3: Ufumu wa Mulungu Udzachotsa Nkhondo ndi Zachinyengo—rs tsa. 377 ndime 3–tsa. 378 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 33

Mph. 10: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba lino, chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyamba m’mwezi wa August. Limbikitsani onse kuti ayambitse maphunziro a Baibulo.

Mph. 15: Muzigwiritsa Ntchito Mafanizo Ophunzitsadi. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 240-243. Pemphani omvera kuti afotokoze mafanizo achidule amene agwiritsapo ntchito mogwira mtima pokambirana ndi eninyumba kapena amene amaphunzira nawo Baibulo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Nyimbo Na. 54 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena