Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/11 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 12/11 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa December 19

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 19

Nyimbo Na. 25 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 17 ndime 10-15 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 11-16 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 13:1-16 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani ‘Timayenda mwa Chikhulupiriro, Osati mwa Zooneka ndi Maso’?—2 Akor. 5:7 (Mph. 5)

Na. 3: Ngati Wina Anena Kuti: “Sikuti Zinthu Zafika Poipa Kwambiri Masiku Ano. Nkhondo, Njala, Zivomezi ndi Umbanda Zakhala Zikuchitika Kuyambira Kalekale”—rs tsa. 268 ndime 6 mpaka tsa. 269 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 54

Mph. 10: Zilengezo. Tchulani mabuku ogawira m’mwezi wa January ndipo chitani chitsanzo chimodzi.

Mph. 15: Mzimu Woyera Umatipatsa Mphamvu Kuti Tizilalikira Molimba Mtima. Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya July 15, 2009, tsamba 22 ndi 23, ndime 12 mpaka 18. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene aphunzirapo.

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana yokambidwa ndi woyang’anira utumiki.

Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena