Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/11 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 12/11 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 26

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 26

Nyimbo Na. 3 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 17 ndime 16-20 ndi bokosi patsamba 181 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 17-23 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 11

Mph. 5: Zilengezo. Kambiranani nkhani yakuti, “Zimene Tingachite Kuti Tizisangalala ndi Nyimbo za Ufumu.”

Mph. 15: Mmene Mungagwiritsire Ntchito Buku la Kukambitsirana za m’Malemba. Nkhani yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 7 ndi 8. Fotokozani mmene mungagwiritsire ntchito mbali zosiyanasiyana za bukuli. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Mph. 15: Kodi Taphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 10:1-35. Kambiranani mmene nkhani imeneyi ingatithandizire mu utumiki.

Nyimbo Na. 18 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena