Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 5/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa May 14

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 14

Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 6 ndime 1-8 ndi bokosi patsamba 44 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 39-43 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 40:1-10 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Anthu Angathe Kulowa mu Mpumulo wa Mulungu?—Aheb. 4:10, 11 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mariya Anali Amayi a Mulungu?—rs tsa. 256 ndime 3 mpaka tsa. 257 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 131

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Mwakutero, Onse Adzadziwa Kuti Ndinu Ophunzira Anga. (Yoh. 13:35) Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya March 1, 2012, patsamba 6. Pemphani omvera kuti anene mmene angagwiritsire ntchito mfundo za m’nkhaniyo pa zochitika zosiyanasiyana.

Mph. 15: “Muzisamala Mukakhala mu Utumiki.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho ndipo ikambidwe ndi woyang’anira utumiki. Fotokozani zimene mpingo ungachite m’gawo lanu potsatira malangizowa.

Nyimbo Na. 74 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena