Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 5/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 21

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 21

Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 6 ndime 9-16 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 44-48 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 46:18-28 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Mariya Anabadwa Ali Wangwiro?—rs tsa. 257 ndime 3 mpaka tsa. 258 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingatani Kuti Tizifesa ‘Motsatira Mzimu wa Mulungu’?—Agal. 6:8 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 95

Mph. 10: Zilengezo. Tchulani mabuku ogawira m’mwezi wa June. Kenako muchite chitsanzo chimodzi chosonyeza mmene tingagawirire bukulo.

Mph. 15: Kodi Achinyamata, Mungachite Upainiya Wothandiza Mukatsekera Sukulu? Nkhani. Fotokozani mwachidule zimene zili m’buku la Gulu, patsamba 113 ndime yoyamba, pamene akufotokoza zimene munthu angachite kuti ayenerere kukhala mpainiya wothandiza. Kenako funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene anachitapo upainiya wothandiza ali pa holide kusukulu. Limbikitsani achinyamata kuti adzachite upainiya wothandiza akatsekera kusukulu.

Mph. 10: “Muzigwiritsa Ntchito Mwaluso ‘Lupanga la Mzimu.’” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 41 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena