Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 10
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 10
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa December 10

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 10

Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 16 ndime 1-7, ndi bokosi patsamba 128 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Zefaniya 1-3–Hagai 1-2 (Mph. 10)

Na. 1: Hagai 1:1-13 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Anthu Anayamba Bwanji Kutsatira Nzeru za Anthu?—rs tsa. 137 ndime 1-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kukhala Ndi Maganizo a Khristu Kumatithandiza Kudziwa Kwambiri Yehova—Mat. 11:27 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 107

Mph. 15: Sukulu ya Utumiki wa Mulungu ya 2013. Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira sukulu. Pogwiritsa ntchito ndandanda ya Sukulu ya Utumiki wa Mulungu ya 2013, kambiranani mfundo zimene mukuona kuti zingathandize kwambiri mpingo wanu. Limbikitsani onse kuti azikonzekera mwakhama nkhani zawo, azipereka ndemanga pa mfundo zazikulu, komanso azigwiritsa ntchito malangizo ochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki amene amaperekedwa mlungu uliwonse.

Mph. 15: “Khalani Mwamtendere ndi Anthu Onse.” Mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuyankha mosayenera mwininyumba wolusa. Kenako muchitenso chitsanzo china chosonyeza wofalitsayo akuyankha moyenera mwininyumba wolusa.

Nyimbo Na. 39 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena