Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 3
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 3
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 3

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 3

Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 8 ndime 8-13 ndi bokosi patsamba 98 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 36-39 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 37:1-17 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chifukwa Chimene Anthu Oukitsidwa Sadzalangidwira Ntchito Zawo Zakale—rs tsa. 111 ndime 4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Akhristu Angaphunzire Chiyani Kwa Abigayeli?—1 Sam. 25:14-35 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 117

Mph. 10: Zimene Munganene Pogawira Magazini a March. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita chitsanzo cha mmene tingagawirire magaziniwo pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zimene zili patsamba lino. Kenako kambiranani chitsanzo cha ulaliki chilichonse kuyambira poyambirira mpaka pamapeto. Pomaliza, funsani omvera kuti afotokoze mmene angagawirire magazini limodzi ndi kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso kumapeto kwa mlungu, pa milungu iwiri yomalizira m’mweziwo.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Lembani Zokhudza Anthu Achidwi.” Kenako apempheni kuti anene zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo.

Nyimbo Na. 95 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena