Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 6
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 6
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 6

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 6

Nyimbo Na. 22 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 2 ndime 12-20 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 1-3 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 2:​16-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Tatsala Pang’ono Kupeza Mpumulo ku Zinthu Zoipa Zimene Satana Amatilimbikitsa Kuchita—rs tsa. 356 ndime 3–tsa. 357 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Kuti Kugonana Konse Ndi Tchimo?—rs tsa. 179 ndime 1–tsa. 180 ndime 3 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 24

Mph. 10: Zimene Munganene Pogawira Magazini a October. Nkhani yokambirana. Pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zimene zili patsamba lino, yambani ndi kuchita chitsanzo cha mmene tingagawirire magaziniwo. Kenako kambiranani zitsanzozi, kuyambira poyamba mpaka pamapeto.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzisiya Funso Loti Mudzakambirane pa Ulendo Wotsatira.” Kenako apempheni kuti anene zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo.

Nyimbo Na. 83 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena